1
Alom 13:14
Nyanja
NTNYBL2025
Ganizilani nikuchita ngati umo Ambuye Yesu Kilisito adachitila.
Compare
Explore Alom 13:14
2
Alom 13:8
Simdadaidwa chindhu ni Mundhu waliyonjhe, nambho mjhikondana. Uyo wamkonda mnjake wakwanilicha thauko la Mnungu.
Explore Alom 13:8
3
Alom 13:1
Kila mundhu wafunika kwavela yawo ali ni ulamulilo aselikali, pakuti alamuli wonjhe achokela kwa Mnungu, ni anyiiwo ali ni ulamulilo aikidwa ni Mnungu
Explore Alom 13:1
4
Alom 13:12
Usiku watha ni usana wawandikila. Chipano tisiye vindhu vonjhe va kumdima, tutenge vida ngati Asikali akonjeka kubulana mu dangalila.
Explore Alom 13:12
5
Alom 13:10
Uyo wamkonda mnjake siwakhoza kumchitila chindhu choipa. Chimwecho chikondi nde kuvela thauko lonjhe.
Explore Alom 13:10
6
Alom 13:7
Apacheni wandhu chijha chifunika apachidwe, yawo afunika kupachidwa malipilo apacheni, yawo afunika kwapacha msongho apachidwe, ni yawo afunika alemekezedwe apacheni ulemu.
Explore Alom 13:7
Home
Bible
Plans
Videos