1
Alom 14:17-18
Nyanja
NTNYBL2025
Pakuti ufumu wa Mnungu osati kudya ni kumwa, nambho ni kukahala ukhalo uwo umkhwadilicha Mnungu, mtendele ni kukondwela uko kupelekedwa ni mzimu wa Mnuungu. Uyo wamtumikila Kilisito mtundu umeneo wamkwadilicha Mnungu, ni wavomelezedwa ni wandhu.
Compare
Explore Alom 14:17-18
2
Alom 14:8
Pakuti tikakhala amoyo tikhala ndande ya kwakwadilicha Ambuye ni tikamwalila timwalila ndande ya kwakwadilicha Ambuye, chipano ngati tikakhala amoyo kapina tikamwalila ife ni wa Ambuye.
Explore Alom 14:8
3
Alom 14:19
Chimwecho tichite vindhu vipelekela tikhale pamojhi kwa mtendele, ni ivo vitithangatila pa kulimbichana.
Explore Alom 14:19
4
Alom 14:13
Chipano tisiye kwalamula okhulupilila anjathu, nambho tilamule kuti tisiye kuchita chalichonjhe icho sichimchitiche okhulupilila mnjathu wachite machimo.
Explore Alom 14:13
5
Alom 14:11-12
Pakuti yalembedwa mmalembo ya Mnungu kuti, “Ngati umo nikhalila Ambuye akamba, Kila mundhu siwanigwadile, kila mmojhi siwakambe mwene kuti ine ni Mnungu” Chipano kila mmojhi wathu siwakambe nghani zake mwene pachogholo pa Mnungu.
Explore Alom 14:11-12
6
Alom 14:1
Mlandileni kwanu mundhu uyo siwadakwime mchikhulupililo, simdayambana nayo ni kuchuchana naye ndande maganizo yake.
Explore Alom 14:1
7
Alom 14:4
Iwe ni yani ata uyese kumlamula mtumiki wa mwina? Wakaima kapina wakagwa ni njhito ya mbuye wake, siwaimenjho nganganga pakuti Ambuye Yesu akhoza kumuimika.
Explore Alom 14:4
Home
Bible
Plans
Videos