1
Matayo 11:28
Nyanja
NTNYBL2025
“Majhani kwa ine, mwaonjhe mchauchika ni kuvutika ni makatundu yolemela, ine sinikuchiteni mpumulile.
Compare
Explore Matayo 11:28
2
Matayo 11:29
Jhichocheni kwa ine ni mnitumikile, mujhiyaluze kwanga, pakuti ine asati okalipa ni nilibe mbuli, namwenjho simpumulile.
Explore Matayo 11:29
3
Matayo 11:30
Pakuti, mayaluzo yayo nikupachani asati yolimba ni yopepuka.”
Explore Matayo 11:30
4
Matayo 11:27
“Atate wanga anipacha vindu vonjhe. Palibe uyo wamjhiwa Mwana nambho Tate wakepe, ni walionjhe yujha Mwana wamsangha kumvunukulila kuti waajhiwe Atate.”
Explore Matayo 11:27
5
Matayo 11:4-5
Yesu wadaayangha, “Pitani ni mkamkambile Yohana yayo mwayaona ni kuyavela. Osapenya apenya, viwete ayenda, amakate alamichidwa, osavela avela, akufa ahyukichidwa ni osauka alalikidwa Uthenga wa Bwino.
Explore Matayo 11:4-5
6
Matayo 11:15
Uyo wali nimakutu yovela, wavele!”
Explore Matayo 11:15
Home
Bible
Plans
Videos