1
Yohana 3:16
Nyanja
NTNYBL2025
Mateyake Amnungu adaakonda wandhu a jhiko la panjhi ni kumchocha Mwana wao wa yokha, kuti kila uyo wamkhulupilila siwadatayika, nambho wakhale ni umoyo muyaya.
Compare
Explore Yohana 3:16
2
Yohana 3:17
Mate yake Amnungu siwadamtume Mwana wake kuti walamule wandhu a pajhiko la panjhi, nambho waombole kupitila mwana wao.
Explore Yohana 3:17
3
Yohana 3:3
Yesu wadamuyangha, “Uzene nikukambila, mundhu ngati siwabadwa kakawili siwakhoza kuuona Ufumu wa Amnungu.”
Explore Yohana 3:3
4
Yohana 3:18
“Uyo wamkhulupilila iye siwa lamulidwa, uyo siwamkhulupilila watho lamulidwa, ndande yosamkhulupilila Mwana wa yokha wa Amnungu.
Explore Yohana 3:18
5
Yohana 3:19
Lamulo lene nde ili, dangalila wajha pajhiko la panjhi, nambho wandhu akonda mdima kusiyana dangalila, ndande vochitika vao ni voipa.
Explore Yohana 3:19
6
Yohana 3:30
Kilisto uyo wasanghidwa ni Amnungu ifunika walemekezedwe kupunda, ine nichike.”
Explore Yohana 3:30
7
Yohana 3:20
Waliyonjhe uyo wachita voipa waliipila dangalila, siwakhoza kujha kudangalila, pakuti siwafuna vindhu vake vijhiwike.
Explore Yohana 3:20
8
Yohana 3:36
Uyo wamkhulupilila Mwana wa Amnungu wali ni umoyo wa muyaya, uyo siwamvela Mwana siwakhala ni umoyo wa muyaya, nambho siwakhale mumkwiyo wa Amnungu.
Explore Yohana 3:36
9
Yohana 3:14
Ngati Musa umo wadaipachikila njoka pamtengo kujha ku phululu, nde umo Mwana wa Mundhu nayo wafunika kupachikidwa
Explore Yohana 3:14
10
Yohana 3:35
Atate amkonda Mwana ni amningha vindhu vonjhe.
Explore Yohana 3:35
Home
Bible
Plans
Videos