1
Mk. 15:34
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Tsono nthaŵi ili 3 koloko, Yesu adafuula kwakukulu kuti, “Eloi, Eloi, lama sabakatani?” Ndiye kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji?”
Compare
Explore Mk. 15:34
2
Mk. 15:39
Mkulu wa asilikali amene adaaimirira pomwepo kuyang'anana naye, ataona kuti Yesu watsirizika akufuula chotero, adati, “Ndithudi, munthuyu adaalidi Mwana wa Mulungu.”
Explore Mk. 15:39
3
Mk. 15:38
Chinsalu chochinga chija cha m'Nyumba ya Mulungu chidang'ambika pakatimpakati, kuyambira pamwamba mpaka pansi.
Explore Mk. 15:38
4
Mk. 15:37
Koma Yesu adafuula kwakukulu, natsirizika.
Explore Mk. 15:37
5
Mk. 15:33
Nthaŵi itakwana 12 koloko masana, padaagwa mdima pa dziko lonse mpaka pa 3 koloko.
Explore Mk. 15:33
6
Mk. 15:15
Choncho Pilato, pofuna kukondwetsa anthuwo, adaŵamasulira Barabasi, nalamula kuti Yesu akwapulidwe. Pambuyo pake adampereka kuti akampachike pa mtanda.
Explore Mk. 15:15