1
Hag. 2:9
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Choncho ulemerero wa Nyumba yachiŵiriyi udzaposa ulemerero wa Nyumba yoyamba ija. Ndipo ndidzakhazikitsa ufulu ndi mtendere pa malo ano. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse.”
Compare
Explore Hag. 2:9
2
Hag. 2:7
Ndidzagwedeza mitundu yonse ya anthu ndipo chuma cha anthu onse chidzabwera, motero Nyumba imeneyi ndidzaidzaza ndi ulemerero waukulu. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse.
Explore Hag. 2:7
3
Hag. 2:4
Komabe Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikuti, usataye mtima iwe Zerubabele, usataye mtima iwe Yoswa, mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, musataye mtima inu nonse. Yambani ntchito, pakuti Ine ndili nanu ndithu.
Explore Hag. 2:4
4
Hag. 2:5
Musachite mantha, popeza kuti mzimu wanga uli pakati panu, monga momwe ndidalonjezera pamene munkatuluka ku Ejipito.
Explore Hag. 2:5