1
AFILIPI 4:6
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.
Compare
Explore AFILIPI 4:6
2
AFILIPI 4:7
Ndipo mtendere wa Mulungu wakupambana chidziwitso chonse, udzasunga mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu.
Explore AFILIPI 4:7
3
AFILIPI 4:8
Chotsalira, abale, zinthu zilizonse zoona, zilizonse zolemekezeka, zilizonse zolungama, zilizonse zoyera, zilizonse zokongola, zilizonse zimveka zokoma; ngati kuli chokoma mtima china, kapena chitamando china, zilingirireni izi.
Explore AFILIPI 4:8
4
AFILIPI 4:13
Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.
Explore AFILIPI 4:13
5
AFILIPI 4:4
Kondwerani mwa Ambuye nthawi zonse: ndibwerezanso kutero, kondwerani.
Explore AFILIPI 4:4
6
AFILIPI 4:19
Koma Mulungu wanga adzakwaniritsa chosowa chanu chilichonse monga mwa chuma chake m'ulemerero mwa Khristu Yesu.
Explore AFILIPI 4:19
7
AFILIPI 4:9
Zimenenso mudaziphunzira, ndi kuzilandira, ndi kuzimva, ndi kuziona mwa ine, zomwezo chitani; ndipo Mulungu wa mtendere adzakhala pamodzi ndi inu.
Explore AFILIPI 4:9
8
AFILIPI 4:5
Kufatsa kwanu kuzindikirike ndi anthu onse. Ambuye ali pafupi.
Explore AFILIPI 4:5
9
AFILIPI 4:12
Ndadziwa ngakhale kupeputsidwa, ndadziwanso kusefukira; konseko ndi m'zinthu zonse ndalowa mwambo wakukhuta, ndiponso wakumva njala; wakusefukira, ndiponso wakusowa.
Explore AFILIPI 4:12
10
AFILIPI 4:11
Si kuti ndinena monga mwa chiperewero, pakuti ndaphunzira ine, kuti zindikwanire zilizonse ndili nazo.
Explore AFILIPI 4:11
Home
Bible
Plans
Videos