1
YESAYA 47:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Watopa mu uphungu wako wambiri; aimirire tsopano openda zam'mwamba, oyang'ana nyenyezi, akuneneratu mwezi ndi mwezi, ndi kukupulumutsa pa zinthu zimene zidzakugwera.
Compare
Explore YESAYA 47:13
2
YESAYA 47:14
Taona, iwo adzakhala ngati ziputu, moto udzawatentha iwo; sadzadzipulumutsa okha kumphamvu za malawi; motowo sudzakhala khala loothako, pena moto wakukhalako.
Explore YESAYA 47:14