1
YESAYA 26:3
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Inu mudzasunga mtima wokhazikika mu mtendere weniweni, chifukwa ukukhulupirirani Inu.
Compare
Explore YESAYA 26:3
2
YESAYA 26:4
Khulupirirani Yehova nthawi yamuyaya, pakuti mwa Ambuye Yehova muli thanthwe lachikhalire.
Explore YESAYA 26:4
3
YESAYA 26:9
Ndi moyo wanga ndinakhumba Inu usiku; inde ndi mzimu wanga wa mwa ine ndidzafuna Inu mwakhama; pakuti pamene maweruziro anu ali pa dziko lapansi, okhala m'dziko lapansi adzaphunzira chilungamo.
Explore YESAYA 26:9
4
YESAYA 26:12
Yehova, mudzatikhazikitsira mtendere; pakuti mwatigwirira ntchito zathu zonse.
Explore YESAYA 26:12
5
YESAYA 26:8
Inde m'njira ya maweruziro anu, Yehova, ife talindira Inu; moyo wathu ukhumba dzina lanu, ndi chikumbukiro chanu.
Explore YESAYA 26:8
6
YESAYA 26:7
Njira ya wolungama ili njira yoongoka; Inu amene muli woongoka, mukonza njira ya wolungama.
Explore YESAYA 26:7
7
YESAYA 26:5
Chifukwa Iye watsitsira pansi iwo amene anakhala pamwamba, mudzi wa pamsanje; Iye wautsitsa, wautsitsira pansi; waugwetsa pansi pa fumbi.
Explore YESAYA 26:5
8
YESAYA 26:2
Tsegulani pazipata, kuti mtundu wolungama, umene uchita zoonadi, ulowemo.
Explore YESAYA 26:2