1
YESAYA 12:2
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Taonani, Mulungu ndiye chipulumutso changa; ndidzakhulupirira, sindidzaopa; pakuti Yehova Mwini ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga, Iye ndiye chipulumutso changa.
Compare
Explore YESAYA 12:2
2
YESAYA 12:3
Chifukwa chake mudzakondwera pakutunga madzi m'zitsime za chipulumutso.
Explore YESAYA 12:3
3
YESAYA 12:5
Muimbire Yehova; pakuti wachita zaulemerero; chidziwike ichi m'dziko lonse.
Explore YESAYA 12:5
4
YESAYA 12:4
Tsiku lomwelo mudzati, Muyamikire Yehova, bukitsani dzina lake, mulalikire machitidwe ake mwa mitundu ya anthu, munene kuti dzina lake lakwezedwa.
Explore YESAYA 12:4
5
YESAYA 12:1
Tsiku lomwelo udzati, Ndikuyamikani inu Yehova; pakuti ngakhale munandikwiyira, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mutonthoza mtima wanga.
Explore YESAYA 12:1
6
YESAYA 12:6
Tafuula, takuwa iwe, wokhala m'Ziyoni, chifukwa Woyera wa Israele wa m'kati mwako ali wamkulu.
Explore YESAYA 12:6