1
HOSEYA 11:4
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndinawakoka ndi zingwe za munthu, ndi zomangira za chikondi; ndinakhala nao ngati iwo akukweza goli pampuno pao, ndipo ndinawaikira chakudya.
Compare
Explore HOSEYA 11:4
2
HOSEYA 11:1
Pamene Israele anali mwana, ndinamkonda, ndinaitana mwana wanga ali m'Ejipito.
Explore HOSEYA 11:1
Home
Bible
Plans
Videos