1
HOSEYA 10:12
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Mudzibzalire m'chilungamo mukolole monga mwa chifundo; limani masala anu, pakuti yafika nthawi ya kufuna Yehova, mpaka afika Iye, navumbitsira inu chilungamo.
Compare
Explore HOSEYA 10:12
2
HOSEYA 10:13
Mwalima choipa, mwakolola chosalungama, mwadya zipatso za mabodza; pakuti watama njira yako ndi kuchuluka kwa anthu ako amphamvu.
Explore HOSEYA 10:13
Home
Bible
Plans
Videos