1
EKSODO 5:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo pambuyo pake Mose ndi Aroni analowa nanena ndi Farao, Atero Yehova, Mulungu wa Israele, Lola anthu anga apite, kundichitira madyerero m'chipululu.
Compare
Explore EKSODO 5:1
2
EKSODO 5:23
Popeza kuyambira kuja ndinafika kwa Farao kulankhula m'dzina lanu, anawachitira choipa anthuwa; ndipo simunalanditsa anthu anu konse.
Explore EKSODO 5:23
3
EKSODO 5:22
Pamenepo Mose anabwerera namka kwa Yehova, nati, Ambuye, mwawachitiranji choipa anthuwa? Mwandituma bwanji?
Explore EKSODO 5:22
4
EKSODO 5:2
Koma Farao anati, Yehova ndani, kuti ndimvere mau ake ndi kulola Israele apite? Sindimdziwa Yehova, ndiponso sindidzalola Israele apite.
Explore EKSODO 5:2
5
EKSODO 5:8-9
Ndipo muziwawerengera njerwa, monga momwe anapanga kale; musachepsapo, popeza achita chilezi; chifukwa chake alikufuula, ndi kuti, Timuke, timphere nsembe Mulungu wathu. Ilimbike ntchito pa amunawo, kuti aigwiritsitse, asasamalire mau amabodza.
Explore EKSODO 5:8-9
Home
Bible
Plans
Videos