YouVersion Logo
Search Icon

EKSODO 5:8-9

EKSODO 5:8-9 BLPB2014

Ndipo muziwawerengera njerwa, monga momwe anapanga kale; musachepsapo, popeza achita chilezi; chifukwa chake alikufuula, ndi kuti, Timuke, timphere nsembe Mulungu wathu. Ilimbike ntchito pa amunawo, kuti aigwiritsitse, asasamalire mau amabodza.

Free Reading Plans and Devotionals related to EKSODO 5:8-9