1
1 AKORINTO 4:20
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti ufumu wa Mulungu suli m'mau, koma mumphamvu. Mufuna chiyani?
Compare
Explore 1 AKORINTO 4:20
2
1 AKORINTO 4:5
Chifukwa chake musaweruze kanthu isanadze nthawi yake, kufikira akadze Ambuye, amenenso adzaonetsera zobisika za mdima, nadzasonyeza zitsimikizo za mtima; ndipo pamenepo yense adzakhala nao uyamiko wake wa kwa Mulungu.
Explore 1 AKORINTO 4:5
3
1 AKORINTO 4:2
Komatu pano pafunika za adindo, kuti munthu akhale wokhulupirika.
Explore 1 AKORINTO 4:2
4
1 AKORINTO 4:1
Chotero munthu atiyese ife, monga atumiki a Khristu, ndi adindo a zinsinsi za Mulungu.
Explore 1 AKORINTO 4:1
Home
Bible
Plans
Videos