1
1 AKORINTO 10:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Sichinakugwerani inu chiyeso koma cha umunthu; koma Mulungu ali wokhulupirika, amene sadzalola inu kuyesedwa koposa kumene mukhoza; koma pamodzi ndi chiyeso adzaikanso populumukirapo, kuti mudzakhoze kupirirako.
Compare
Explore 1 AKORINTO 10:13
2
1 AKORINTO 10:31
Chifukwa chake mungakhale mudya, mungakhale mumwa, mungakhale muchita kanthu kena, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu.
Explore 1 AKORINTO 10:31
3
1 AKORINTO 10:12
Chifukwa chake iye wakuyesa kuti ali chilili, ayang'anire kuti angagwe.
Explore 1 AKORINTO 10:12
4
1 AKORINTO 10:23
Zinthu zonse ziloleka; koma sizipindula zonse. Zinthu zonse ziloleka; koma sizimanga zonse.
Explore 1 AKORINTO 10:23
5
1 AKORINTO 10:24
Munthu asafune zake za iye yekha, koma za mnzake.
Explore 1 AKORINTO 10:24
Home
Bible
Plans
Videos