1
Yeremiya 24:7
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndidzawapatsa mtima woti andidziwe kuti ndine Yehova. Adzakhala anthu anga ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo, chifukwa adzabwerera kwa Ine ndi mtima wawo wonse.
Compare
Explore Yeremiya 24:7
2
Yeremiya 24:6
Ndidzaonetsesa kuti ndiwachitire zabwino ndipo ndidzabwera nawonso ku dziko lino. Ndidzawamanga osati kuwapasula; ndidzawadzala osati kuwazula.
Explore Yeremiya 24:6