Inu Yehova, ndinu mphamvu yanga ndi linga langa,
pothawirapo panga nthawi ya masautso,
anthu a mitundu yonse adzabwera kwa Inu
kuchokera ku mathero onse a dziko lapansi ndipo adzanena kuti,
“Makolo anthu anali ndi milungu yonama,
anali ndi mafano achabechabe amene sanawathandize.