1
Yesaya 7:14
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Nʼchifukwa chake Ambuye mwini adzakupatsani chizindikiro: Onani, namwali adzakhala woyembekezera ndipo adzabala mwana wamwamuna, ndipo mwanayo adzamutcha Imanueli.
Compare
Explore Yesaya 7:14
2
Yesaya 7:9
Dziko la Efereimu limadalira Samariya ndipo Samariya amadalira mwana wa Remaliya basi. Mukapanda kulimbika pa chikhulupiriro chanu, ndithu simudzalimba konse.’ ”
Explore Yesaya 7:9
3
Yesaya 7:15
Azidzadya chambiko ndi uchi, mpaka atadziwa kukana choyipa ndi kusankha chabwino.
Explore Yesaya 7:15