1
Ezekieli 43:4-5
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ulemerero wa Yehova unalowa mʼNyumba ya Mulungu kudzera pa chipata choyangʼana kummawa. Tsono Mzimu unandinyamula nundilowetsa mʼbwalo lamʼkati, ndipo ulemerero wa Yehova unadzaza Nyumba ya Mulungu.
Compare
Explore Ezekieli 43:4-5