YouVersion Logo
Search Icon

Ezekieli 43:4-5

Ezekieli 43:4-5 CCL

Ulemerero wa Yehova unalowa mʼNyumba ya Mulungu kudzera pa chipata choyangʼana kummawa. Tsono Mzimu unandinyamula nundilowetsa mʼbwalo lamʼkati, ndipo ulemerero wa Yehova unadzaza Nyumba ya Mulungu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Ezekieli 43:4-5