1
Ezekieli 16:49
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“ ‘Tsono tchimo la mʼbale wako Sodomu linali ili: Iye ndi ana ake aakazi ankanyadira kuchuluka kwa chakudya ndi chuma chawo. Koma sanalabadireko kuthandiza osauka ndi aumphawi.
Compare
Explore Ezekieli 16:49
2
Ezekieli 16:60
Komabe, Ine ndidzakumbukira pangano limene ndinachita nawe mʼmasiku a unyamata wako, ndipo ndidzakhazikitsa pangano losatha ndi iwe.
Explore Ezekieli 16:60