Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

MATEYU 8:26

MATEYU 8:26 BLPB2014

Ndipo ananena Iye kwa iwo, Muli amantha bwanji, okhulupirira pang'ono inu? Pomwepo Iye anauka, nadzudzula mphepo ndi nyanja, ndipo panagwa bata lalikulu.