Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

MATEYU 13:19

MATEYU 13:19 BLPB2014

Munthu aliyense wakumva mau a Ufumu, osawadziwitsai, woipayo angodza, nakwatula chofesedwacho mumtima mwake. Uyo ndiye wofesedwa m'mbali mwa njira.