1
GENESIS 50:20
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma inu, munandipangira ine choipa; koma Mulungu anachipangira chabwino, kuti kuchitike monga lero, kupulumutsa amoyo anthu ambiri.
Linganisha
Chunguza GENESIS 50:20
2
GENESIS 50:19
Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Musaope; pakuti ndili ine kodi m'malo a Mulungu?
Chunguza GENESIS 50:19
3
GENESIS 50:21
Ndipo tsopano musaope; ine ndidzachereza inu, ndi ana anu ang'ono. Ndipo anawatonthoza iwo mitima yao, nanena nao mokoma mtima.
Chunguza GENESIS 50:21
4
GENESIS 50:17
Muziti chotero kwa Yosefe, Mukhululukiretu tsopano kulakwa kwa abale anu, ndi kuchimwa kwao, chifukwa kuti anakuchitirani inu choipa; tsopano mutikhululukiretu kulakwa kwa akapolo a Mulungu wa atate wanu. Ndipo Yosefe analira pamene iwo ananena ndi iye.
Chunguza GENESIS 50:17
5
GENESIS 50:24
Yosefe ndipo anati kwa abale ake, Ndilinkufa ine, koma Mulungu adzaonekera kwa inu, adzakuchotsani inu m'dziko muno kubwera kunka ku dziko limene analumbirira kwa Abrahamu ndi kwa Isaki, ndi kwa Yakobo.
Chunguza GENESIS 50:24
6
GENESIS 50:25
Ndipo Yosefe analumbiritsa ana a Israele kuti, Mulungu adzaonekera kwa inu ndithu, ndipo mudzakwera nao mafupa anga kuchokera kuno.
Chunguza GENESIS 50:25
7
GENESIS 50:26
Ndipo anafa Yosefe, anali wa zaka zana limodzi ndi khumi; ndipo anakonza thupi lake ndi mankhwala osungira, ndipo anamuika iye m'bokosi m'Ejipito.
Chunguza GENESIS 50:26
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video