1
EKSODO 1:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma anamwino anaopa Mulungu, ndipo sanachite monga mfumu ya Aejipito inawauza, koma analeka ana amuna akhale ndi moyo.
Linganisha
Chunguza EKSODO 1:17
2
EKSODO 1:12
Koma monga momwe anawasautsiramo, momwemo anachuluka, momwemonso anafalikira. Ndipo anavutika chifukwa cha ana Israele.
Chunguza EKSODO 1:12
3
EKSODO 1:21
Ndipo kunatero kuti, popeza anamwino anaopa Mulungu, Iye anawamangitsira mabanja.
Chunguza EKSODO 1:21
4
EKSODO 1:8
Pamenepo inalowa mfumu yatsopano m'ufumu wa Ejipito, imene siinadziwa Yosefe.
Chunguza EKSODO 1:8
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video