1
2 AKORINTO 13:5
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Dziyeseni nokha, ngati muli m'chikhulupiriro, dzitsimikizeni nokha. Kapena simuzindikira kodi za inu nokha kuti Yesu Khristu ali mwa inu? Mukapanda kukhala osatsimikizidwa.
Linganisha
Chunguza 2 AKORINTO 13:5
2
2 AKORINTO 13:14
Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.
Chunguza 2 AKORINTO 13:14
3
2 AKORINTO 13:11
Chotsalira, abale, kondwerani. Muchitidwe angwiro; mutonthozedwe; khalani a mtima umodzi, khalani mumtendere; ndipo Mulungu wa chikondi ndi mtendere akhale pamodzi ndi inu.
Chunguza 2 AKORINTO 13:11
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video