لوگوی اپلیکیشن کتاب مقدس
كتاب‌ مقدسبرنامه‌های مطالعهویدیوها
دانلود برنامه
انتخاب زبان
ایکن جستجو

آیات محبوب کتاب مقدس از Hag. 2

1

Hag. 2:9

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Choncho ulemerero wa Nyumba yachiŵiriyi udzaposa ulemerero wa Nyumba yoyamba ija. Ndipo ndidzakhazikitsa ufulu ndi mtendere pa malo ano. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse.”

مقایسه

Hag. 2:9 را جستجو کنید

2

Hag. 2:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Ndidzagwedeza mitundu yonse ya anthu ndipo chuma cha anthu onse chidzabwera, motero Nyumba imeneyi ndidzaidzaza ndi ulemerero waukulu. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse.

مقایسه

Hag. 2:7 را جستجو کنید

3

Hag. 2:4

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Komabe Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikuti, usataye mtima iwe Zerubabele, usataye mtima iwe Yoswa, mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, musataye mtima inu nonse. Yambani ntchito, pakuti Ine ndili nanu ndithu.

مقایسه

Hag. 2:4 را جستجو کنید

4

Hag. 2:5

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Musachite mantha, popeza kuti mzimu wanga uli pakati panu, monga momwe ndidalonjezera pamene munkatuluka ku Ejipito.

مقایسه

Hag. 2:5 را جستجو کنید

باب‌ قبلی
باب بعدی
یوورژن

به چالش کشیدن و تشویق هر روزه شما برای ایجاد رابطه صمیمی تر با خدا .

خدمت

دربارهٔ

بلاگ

مطبوعات

هدایا

لینک‌های مفید

پشتیبانی

ترجمه‌های کتاب‌مقدس

کتاب‌ مقدس صوتی

ترجمه‌های موجود کتاب‌مقس

آیۀ روز


فارسی

©2026 یوورژن

قوانین حفظ حریم شخصیشرايط
برنامه افشای آسیب پذیری
فیس‌بوکتویتراینستاگرامبرنامه یوتیوببرنامه پین ترست