YouVersion Logo
Search Icon

Matayo 24:9-11

Matayo 24:9-11 NTNYBL2025

“Ndiipo sakugwileni kuti mvutichidwe ni kuphedwa. Wandhu a maiko yonjhe siyakuipileni ndande anyiimwe ni oyaluzidwa wanga. Nyengo imeneyo, wandhu ambili yawo anikhulupilila siasiye kunikhulupilila, ni kung'anamukana ni kuipilana. Siachokele alosi ambili amthila, ni anyiiwo siwanyenge wandhu ambili.

Free Reading Plans and Devotionals related to Matayo 24:9-11