YouVersion Logo
Search Icon

Yohana 8:10-11

Yohana 8:10-11 NTNYBL2025

Yesu yapo wadaima wadamfunjha wamkaziyo, “Alikuti wajha wandhu akupacha mlandhu? Palibe waliyonjhe uyo wakulamula?” Wamkazi mmeneyo wadayangha, “Wakulu, palibe waliyonjhe!” Ndiipo Yesu wadamkambila, “Ata ine sinikulamula. Mapita siudachitanjho machimo.”