YouVersion Logo
Search Icon

Vichito 14

14
Poolo ni Banaba alalikila wandhu ku Ikonio
1Kujha kumujhi wa Ikonio kudachitika vindhu ngati vijha vidachitika ku Antiyokiya. Poolo ni Banaba adapita munyumba yokomanilana Ayahudi ngati umo lili khalidwe lao ni kukamba kwa mbhavu mbaka Ayahudi ambili ni osati Ayahudi adamkhulupilila Yesu. 2Nambho Ayahudi yawo sadakhulupilalile, adaakwilizila wandhu osati Ayahudi waipile Poolo ni Banaba. 3Atumwi adakhla malo yajha kwa ndhawi yaitali, niakamba popande mandha nghani za Ambuye, uyo wadachimikiza uthenga wa ubwino wake pa kwaakhozecha kuchita vizindikilo ni vodabwicha. 4Wandhu a mmujhi ujha adapatukana, anjake adali kwa Ayahudi ni anjake adali kwa atumwi.
5Ndiipo Ayahudi wina ni osati Ayahudi, pamojhi ni achogoleli, adaganiza kwaavuticha atumwi ni kwaaponya miyala. 6Yapo atumwi adaona chimwechi adathawila ku jhiko la Lisitila ni Delibe, kumijhi ya Likoniya ni malo yayo yalunjana nayo. 7Anyiiwo adakhala kumeneko ni adalalikila uthenga wabwino.
Poolo ni Banaba ku Lisitila ni Delibe
8Mumujhi wa Lisitila kudali wammuna mmojhi uyo wadali ndendele kuyambila kubadwa ni siwadakhoze kuyenda. 9Mundhu mmeneyo wadamvela Poolo yapo wamalalikila, naye Poolo yapo wadampenyechecha, wadaona kuti mundhu mmeneyo wakhulupilila ni wakhoza kulamichidwa, 10wadamkambila kokweza mvekelo, “Ima kwa miyendo yako!” Pampajha yujha Mundhu wadalumbha ni kuyamba kuyenda. 11Gulu yapo lidaona ivo wadachita Poolo, adayamba kubula phokoso kwa chimkambo chao cha Chilikaoniya niakamba, “Minungu yali ngati wandhu yatichikila ife!” 12Adampacha Banaba Zeu jhina la mnungu wao wamkulu, ni Poolo adampacha jhina Helime pakuti Poolo nde uyo wadali wokamba wamkulu. 13Mjhukulu wa mnungu Zeu, uyo nyumba yake idali kubwalo pang'ono kwa mujhi, wadajha ni ng'ombe za mbhongo ni maduwa pakhomo la mujhi, pakuti iye ni gulu la wandhu amafuna kuchocha njhembe kwa atumwi.
14Yapo Poolo ni Banaba adavela icho amafuna kuchita wandhu wajha, adang'amba njhalu zao kulangiza kukana ganizo limenelo ni kulowa pa gulu la wandhu kwa msanga, adabula phokosa pokamba, 15“Ndande yanji mchita chimwechi? Ife nafenjho ni wandhupe ngati anyiimwe! Tili pano kuuzila Uthenga Wabwino kuti musiye kulambila viboliboli ni kumng'anamukila Mnungu wamoyo, uyo wadaumba kumwamba, jhiko lapanjhi, nyanja ni vindhu vonjhe ivo vili mkati mwake. 16Kale Mnungu wadaasiya wandhu wonjhe osati Ayahudi achite ivo amavifuna. 17Nambho iye Mnungu siwadaleke kujhilangiza kwa kwachitila vindhu vabwino. Iye wakupachani mvula kuchokela kumwamba ni vokolola pa ndhawi yabwino. Wakupachani vakudya ni kujhaza kukondwa mitima yanu.” 18Pokamba chimwecho, Banaba ni Poolo adakhoza kwaachekeleza wandhu wajha kwa vuto siadaachochela njhembe.
19Pambuyo pandhawi adajha ayahudi wina kuchokela ku Antiyokia ni Ikoniya, wadaanyenga wandhu wajha kuti amponye miyala Poolo, ni kumkwekwetela kubwalo kwa mujhi, uku niaganiza kuti wamwalila. 20Nambho yapo wokhulupilila adasonghana kumzungululila iye Poolo, wadaima ni kupitanjho ku mujhi ujha. Siku lochatila iye pamojhi ni Banaba adapita ku Delibe.
Poolo ni Banaba abwelanjho ku mujhi wa Antiokia uwo uli mu Siliya
21Poolo ni Banaba adalakila uthenga wabwino mu mujhi wa Delibe ni wandhu ambili adamkhulupipilila Yesu. Adamanga ulendo kupita ku mijhi ya Lisitila ni Ikoniya ni mujhi wa Antiokia ya Pisidiya. 22Wadaalimbicha oyaluzidwa amijhi imeneyo ni kwaathila mitima kuti ayendekele kukhulupilika mu chikhulupililo. Wadaaonya niakamba, “Wandhu sativute tikali osalowe mu Ufumu wa Mnungu.” 23Poolo ni Banaba yapo amayenda mu magulu yonjhe ya wandhu amkhulupilila Kilisito, amasangha achogoleli, ni kwaaika mmanja mwa Ambuye uyo anyiiwo adamkhulupilila, adamanga kudya ni adapembhela, Mnungu waasunge.
24Ndiipo adapita pakati pa Pisidiya ni kulowa ku mujhi wa Pamfiliya. 25Pambuyo pa kwaalalikila wandhu Uthenga Wabwino ku Peliga, adachoka ni kupita ku Ataliya. 26Adaendekela ni ulendo kwa Sitima kubwela ku Antiokia ya Siliya, kujha poyamba adapembheledwa ni Mnungu wadapacha mwawi ndande ya njhito iyo adaikwanilicha.
27Yapo adafika ku Antiokia, adaasonghanicha pamojhi wandhu amkhulupila Kilisito ni kwaakambila yonjhe yayo wachita Mnungu kupitila anyiiwo, ni umo waadakhozecha wandhu osati Ayahudi amkhulupilile Kilisito. 28Nawo adakhala nyengo yaitali kumeneko pamojhi ni wokhulupilila.

Currently Selected:

Vichito 14: NTNYBL2025

Highlight

Share

Copy

None

Want to have your highlights saved across all your devices? Sign up or sign in