YouVersion Logo
Search Icon

Zek. 8:13

Zek. 8:13 BLY-DC

Inu mabanja a Yuda ndi Israele, kale munali chizindikiro cha matemberero pakati pa mitundu ina ya anthu. Koma tsopano ndidzakupulumutsani ndipo mudzakhala chizindikiro cha madalitso. Musaope, limbani mtima.

Free Reading Plans and Devotionals related to Zek. 8:13