YouVersion Logo
Search Icon

Zek. 4:6

Zek. 4:6 BLY-DC

Tsono iye adandiwuza kuti ndidziŵitse Zerubabele uthenga wa Chauta wakuti, “Inde udzapambana, koma osati ndi nkhondo kapena ndi mphamvu, koma ndi mzimu wanga.