YouVersion Logo
Search Icon

Zek. 4:10

Zek. 4:10 BLY-DC

Pakali pano anthuwo ndi okhumudwa kuwona kuti ntchito sikufulumira. Koma akadzamuwona Zerubabele atatenga mwala wotsiriza uja m'manja mwake, pamenepo adzakondwa. “Nyale zisanu ndi ziŵiri ndi maso a Chauta amene akunka nayang'anayang'ana pa dziko lonse lapansi.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Zek. 4:10