YouVersion Logo
Search Icon

Zek. 12:10

Zek. 12:10 BLY-DC

“Tsono anthu a pa banja la Davide ndi anthu onse a ku Yerusalemu ndidzaŵadzaza ndi mtima wachifundo ndi wakupemphera. Motero adzati atamuyang'ana amene adambaya, adzamlira kwabasi monga muja amamlirira mwana akakhala mmodzi yekha. Adzamliradi kwambiri monga muja amamlirira mwana wachisambamu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Zek. 12:10