YouVersion Logo
Search Icon

Mk. 2:17

Mk. 2:17 BLY-DC

Yesu atamva zimenezo adaŵayankha kuti, “Anthu amene ali bwino sasoŵa sing'anga ai, koma amene akudwala. Inetu sindidabwere kudzaitana anthu olungama, koma anthu ochimwa.”