YouVersion Logo
Search Icon

Mk. 16:4-5

Mk. 16:4-5 BLY-DC

Koma poyang'anitsitsa adaona kuti chimwalacho achigubuduza kale; tsonotu chinali chachikuludi. Ataloŵa m'mandamo adaona mnyamata wakhala pansi mbali ya ku dzanja lamanja, atavala mkanjo woyera. Azimaiwo adadzidzimuka.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mk. 16:4-5