YouVersion Logo
Search Icon

Mk. 14:23-24

Mk. 14:23-24 BLY-DC

Kenaka adatenga chikho, nathokoza Mulungu, nkuchipereka kwa ophunzirawo, naamwa onse. Ndipo adaŵauza kuti, “Aŵa ndi magazi anga otsimikiza Chipangano cha Mulungu. Magazi ameneŵa ndiŵakhetsa chifukwa cha anthu ochuluka.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mk. 14:23-24