YouVersion Logo
Search Icon

Mk. 13:8

Mk. 13:8 BLY-DC

Mitundu yosiyanasiyana idzaukirana, maiko osiyanasiyana adzamenyana nkhondo. Kudzachita zivomezi ku malo osiyanasiyana, ndipo kudzakhala njala. Tsono zonsezitu nkuyamba chabe kwa mavuto.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mk. 13:8