YouVersion Logo
Search Icon

Mk. 13:11

Mk. 13:11 BLY-DC

Tsono akadzakugwirani ndi kukuperekani ku mlandu, musadzaderetu nkhaŵa nkumaganiza kuti, ‘Kodi tikanene chiyani?’ Ai, inu mukangonena zimene Mulungu akakuuzeni pa nthaŵi imeneyo. Pajatu odzalankhula sindinu ai, koma Mzimu Woyera.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mk. 13:11