YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 8:26

Mt. 8:26 BLY-DC

Apo Yesu adaŵafunsa kuti, “Bwanji mukuchita mantha, inu anthu a chikhulupiriro chochepa?” Atatero adaimirira nkudzudzula mphepoyo ndi nyanjayo, kenaka padagwa bata lalikulu ndithu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 8:26