YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 7:3-4

Mt. 7:3-4 BLY-DC

Umaoneranji kachitsotso kamene kali m'maso mwa mnzako, koma osaganizako za chimtengo chimene chili m'maso mwako momwe? Ungamuuze bwanji mbale wako kuti, ‘Taima ntakuchotsa kachitsotso kali m'maso mwakoka,’ pamene m'maso mwako momwe muli chimtengo?

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 7:3-4