YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 7:15-16

Mt. 7:15-16 BLY-DC

“Chenjera nawoni aneneri onyenga. Amadza kwa inu ali ndi maonekedwe ofatsa ngati nkhosa, koma m'kati mwao ndi mimbulu yolusa. Mudzaŵadziŵira zochita zao. Kodi mitengo yaminga nkubala mphesa? Kodi mitula nkubala nkhuyu?

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 7:15-16