YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 5:13

Mt. 5:13 BLY-DC

“Inu ndinu mchere wa dziko lapansi. Koma ngati mcherewo watha mphamvu, mphamvu zakezo nkuzibwezeranso nchiyani? Ulibenso ntchito mpang'ono pomwe, koma kungoutaya kunja basi, anthu nkumauponda.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 5:13