YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 24:9-11

Mt. 24:9-11 BLY-DC

“Pambuyo pake anthu adzakuperekani kuti mukazunzidwe, kenaka adzakuphani. Anthu a mitundu yonse ya anthu adzadana nanu chifukwa cha Ine. Pa nthaŵi imeneyo ambiri adzataya chikhulupiriro chao, azidzaperekana nkumadana. Kudzaoneka aneneri onama ambiri, amene azidzasokeza anthu ambiri.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 24:9-11