YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 24:6

Mt. 24:6 BLY-DC

Mudzamva phokoso la nkhondo za kufupi kuno ndi mphekesera za nkhondo zakutali. Ndiye inu musadzade nkhaŵa. Zimenezi zidzayenera kuchitika, koma sindiye kuti chimalizo chija chafika kale ai.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 24:6