YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 24:24

Mt. 24:24 BLY-DC

Chifukwa kudzaoneka anthu onama omanena kuti ‘Ndine Khristu uja,’ kapena kuti, ‘Ndine mneneri.’ Anthuwo azidzachita ntchito zamphamvu ndiponso zinthu zozizwitsa, kuti ngati nkotheka asokeze ngakhale osankhidwa a Mulungu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 24:24