Mt. 24:12-13
Mt. 24:12-13 BLY-DC
Tsono popeza kuti zoipa zizidzachulukirachulukira, chikondi chizidzacheperachepera pakati pa anthu. Koma yemwe adzalimbikire mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke.
Tsono popeza kuti zoipa zizidzachulukirachulukira, chikondi chizidzacheperachepera pakati pa anthu. Koma yemwe adzalimbikire mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke.