YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 23:25

Mt. 23:25 BLY-DC

“Muli ndi tsoka, inu aphunzitsi a Malamulo ndi Afarisi, anthu achiphamaso! Mumatsuka kunja kwa chikho ndi kwa mbale koma m'kati mwake m'modzaza ndi nzeru zakuba, ndi zaumbombo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 23:25