YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 19:29

Mt. 19:29 BLY-DC

Motero aliyense wosiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena atate, kapena amai, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine, ameneyo adzalandira zonsezo mochuluka kwambiri koposa kale, kenaka adzalandira moyo wosatha.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 19:29